Misa Yothokoza ndi Chaka Cha Macheza Cha Amayi a Mpingo waKatolika mu Arkidayosizi ya Lilongwe (M’Zithunzi)


Wojambula ndi Eric Norman Mkwaira



Wojambula ndi Eric Norman Mkwaira







Fr. Silvestro Zanardi (bambo Silvio) anabadwa pa 28th December 1940 ku Bergamo, m’dziko la Italy. Choncho, bambo Silvio amwalira pa 5 June, 2024 ali ndi zaka  84.
Moyo wa unsembe
Bambo Silvio anadzodzedwa unsembe pa 28th June 1967 kwawo ku Italy. Iwo amwalira ali ndi zaka 57 mu unsembe. Mu zaka zimenezi, bambo Silvio atumikira Mulungu ngati wansembe motere:
Iwo anatumikira ngati bambo mfumu pa St. John (Msamba) Catholic Parish kuyambira mu chaka cha 2001 mpaka 2012 pamene anapereka udindo wa bambo mfumu kwa Fr. John Paul Somanje. Mu mbiri ya parishi yathu, Bambo Silvio ndi wakhala bambo mfumu kwa zaka zochuluka.
Atapumula pa udindo wa bambo mfumu mu chaka cha 2011, bambo Silvio anapitiriza kutumikira parishi ngati wansembe ongothandiza makamaka ma outstation. Iwo anapitiriza kugwira ntchito yawo ya unsembe yopereka masakaramenti (ubatizo, ukwati, kulapa, kudzoza), kuchita Misa lamulungu/mkati mwa sabata/pamaliro komanso chitukuko. Chitukuko chachikulu chomwe agwira ali wansembe othandiza ndi kumanga tchalitchi latsopano kwa nkhukwa.
Tidzawakumbira bwanji?
Tipemphe mulungu kuti ntchito zabwino zomwe Bambo Silvio anagwira ali moyo zimuperekeze ku paradizo kwao.

There was an ululation on Saturday 20th of July 2024 at Our Lady of Hope, Chiphaso Parish in Kasungu District, as the Clergy and the laity celebrated and witnessed the ordination of Deacon Selso Magwaza and Deacon Blessings Siliya of the order of Carmelite Friars.
The cerebration started with a Mass which was presided over by the Auxiliary Bishop for the Catholic Archdiocese of Lilongwe, Rt. Rev. Vincent Mwakhwawa, since his Consecration as an Auxiliary Bishop on 20th January 2024, and with his Grace Archbishop George Desmond Tambala of the Archdiocese.
In his speech, Bishop Vincent Mwakhwawa urged the new ordained priests to save the church with zeal and also to be prayerful.
Bishop Mwakhwawa also asked the new Priests to take part in bringing together and provide awareness to Christians, on the ongoing phase three of Synod of Lilongwe discussions.
“We are all aware that as Archdiocese we are on a wave three of our discussions concerning Synod of Lilongwe, and there is a need for all Christians in the Archdiocese to take part on this ongoing discussion as it will help in developing different areas of development in our Archdiocese,” said Bishop Mwakhwawa.
The Bishop also encouraged the new Priests to give hope to people, as they face different challenges in their everyday life.
On his part, the new ordained Father Selso Magwaza, praised God for the Calling, and he has also urged the youths to listen to God’s call.
“My message to the Youths is that they have to listen to God’s call, and they have to be active is serving the Church,” said Fr. Magwaza.
Fr. Magwaza will be serving at Formation House for the Carmelite Friars in Balaka district while Fr. Siliya will be serving at Our Lady of Mount Carmel, Kapiri Parish in Mchinji.

By Titus Jata Phiri


Brian Odiambo, Director of Social Services

Dr Jeremoni Chiundira, Likuni Mission Hospital Chief Medical Officer

Teresa Garolera, Active Africa president
