CHIKONDWERERO CHA SILVER JUBILEE YA FR. KAPIRI (MZITHUNZI)

Mwambo wa nsembe ya Misa yokondwelera kuti bambo Peter Kapiri Mwale akwanitsa zaka 25 akutumikira ngati wa nsembe (1999 – 2024).

Mwambo wa nsembe ya Misayi unatsogoleredwa ndi ambuye George Desmond Tambala a Arkidayosizi ya Katolika ya Lilongwe pa 21 September 2024 ku Parishi ya St. Francis of Assisi, Kanengo.

Mwazina, bambo Kapiri anabwerezaso malonjezo awo a unsembe ndi kulonjeza kupitilira kutumikira mulungu mwa totomoyo.

Izi ndi zina mwa zithunzi zomwe Eric Norman Mkwaira wa Radio Alinafe anajambula pa mwambowu.

Vie all pictures here.